@jnw.nyasaland.off: Anduna azachuma Hon Mwananveka akuti Malawi ili ndi ngongole ya 21.6 trillion Ngongole imeneyi yawonjezeleka kuchokela pa 4 trillion mu chaka cha 2019 #MalawiPolitics #fypシ゚viralシfypシ゚ #fyp #malawitiktok🇲🇼
nde wina afuna DPP kuti ikonze zithu kwa mwezi aaaaah 🥺🥺
2025-11-21 14:04:18
134
Elizabeth🥰 :
🤣🤣🤣 akazati km iwe🤣🤣
2025-11-21 22:58:56
0
DR LOUISCHEN :
koma iwe for me😂😂😂
2025-11-21 13:04:34
63
philes mbozanani :
Chifukwa chake amubweza ku Tanzania aaah
2025-11-21 13:20:47
82
engees :
chipanicho osangochithesa bwanj??
2025-11-21 12:34:57
28
DJ_2REAL :
"koma iwe"😂😂😂😭
2025-11-21 17:48:18
29
Barbie♤ :
fromu whati?
koma iwe!!😭😂😂I'm on the floor
2025-11-21 14:11:48
58
Nicholas Moyo :
mukumbukire kut 5 year Malawi tadusa munyengo zowawa komaso ndalama yagwa kambilimbiri so izi ziyenekera kuchitika
2025-11-21 16:45:49
6
Zikani Joyah :
"FROMU WHATI"
2025-11-21 16:27:18
107
DeBlessing :
no time to point fingers tiyeni tikonze dzikoli basi zanunkha zanunkha basi
2025-11-21 18:49:46
3
Nara TK Likharu :
😂😂😂 the background noise 🤣🤣🤣
2025-11-21 17:28:53
5
Frankie :
Lets not play blame game here, Politicians whether Chakwera kaya APM they don't care about the welfare of the actual citizens. politics is a game and they gamble with human lives